Azanyengo ati kugwa mvula ya mphamvu kuyambira lachitatu likudzali

Pamene madera amchigawo chapakati komanso kumwera kwa dziko lino kuli nga’mba, tsopano nthambi yoona za nyengo ndi kusintha kwa nyengo yati kuyambira lachitatu pa 13 December,  a Malawi  ayembekezere kulandira mvula ya mphamvu. Malingana ndi chikalata chomwe nthambiyi yatulutsa kudzera mwa m’neneri wa nthambiyi a Yobu Kachiwanda ati mvula ikuyembekezereka kugwa mmadera ochuluka mdziko lino. […]

The post Azanyengo ati kugwa mvula ya mphamvu kuyambira lachitatu likudzali appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください