Iyi ndi chorus ya nyimbo ya oyimba otchuka otchedwa Jetu yomwe wangotulutsa kumene maola ochepa apitawa. Nyimboyi yomwe dzina lake ndi chakwaza, ikuonetsa kuti mzimayiyu anali ndi chibwenzi dzina lake John ndipo chinatha mosakhala bwino zomwe zinapangitsa kuti asweke mtima. ” Kale unandiuza suli ready za chikondi sizingatheke m’malo mwake mzanga analowa fisi,” ikutero mbali […]
The post Ayi chonde pitani khomo la mtima wanga ndatseka- Watero Jetu appeared first on Malawi 24.