Asilamu atentha dambwe ku Kasungu

Asilamuwo atentha dambwe m’mudzi wa Mchinga kwa mfumu Njombwa ku Kasungu chifukwa gule wamkulu anagwira mwana wa mtsogoleri wachisilamu kukalowa naye ku dambweko. Malingana ndi wailesi ya Zodiak, gule wamkulu anagwira mwana wa mtsogoleri wachisilamu kukalowa naye ku dambweko ndipo izi ndi zomwe zinayambitsa mkangano pakati pa magulu awiriwa. A Paul Dickson omwe anaona izi […]

The post Asilamu atentha dambwe ku Kasungu appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください