Apolisi ayamba kunjata anthu ogulitsa mowa wa “Ambuye Tengeni”

Kwachema kwa Manase ku Blantyre pamene apolisi ayamba kunjata anthu onse omwe akugulitsa mowa omwe ndi owopsa ndipo ukutchulidwa ndi mayina monga: Ambuye tengeni, magaga, komanso taya njinga omwe pakadali pano waphapo anthu asanu (5). Malingana ndi mneneri wa apolisi m’chigawo chakummwera, a Joseph Sauka, ati ntchitoyi ili mkati pamene apolisi afikakale kuderali komwe akulanda […]

The post Apolisi ayamba kunjata anthu ogulitsa mowa wa “Ambuye Tengeni” appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください