Apolisi athila utsi okhetsa misozi kutabuka zipolowe ku mpingo wa Mibawa CCAP

Ku mpingo wa Mibawa CCAP omwe uli pansi pa sinodi ya Blantyre kunabuka nkangano mpingowu utakana kuyimbila maliro a membala wake ponena kuti amamwa mowa. Malingana ndi lipoti ya MBC, abale a munthu omwalirayo komanso ena omwe amakhala mozungulira derali anayamba kugenda komanso kufuna kutentha tchalitchi cha Mibawa CCAP ponena kuti chakana mkhristu wawo. Akuluakulu […]

The post Apolisi athila utsi okhetsa misozi kutabuka zipolowe ku mpingo wa Mibawa CCAP appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください