Apolisi  apulumutsa fetereza ndi chimanga ku mbava

Apolisi ku  mu Mzinda Lilongwe anjata anthu asanu ndi anayi (9) powaganizira kuti ndi mbava zomwe zimafuna kuba fetereza ndi chimanga ku kampani ya za ulimi ya  Agricultural Research and Extension Trust (ARET). Malingana ndi mneneli wa polisi  ku Lilongwe a Hastings Chigalu ati anthuwa ananyamula zida zoopsa kuphatikizapo zikwanje ndi zitsulo zomwe amafuna kukatsekulira […]

The post Apolisi  apulumutsa fetereza ndi chimanga ku mbava appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください