A Malondera Aphungu a nyumba ya malamulo mdziko muno apempha boma kuti lilingalire zowagulira ma khotholo kuti asamanyowe pomwe akukalowa mnyumbayi kuchokera pa malo osungira ma galimoto. Izi ndimalingana ndi phungu wadera lakummwera chakummawa kwa boma la Lilongwe a Steven Malondera omwe anapititsa nkhaniyi ku nyumba ya malamulo pazokambirana za lachitatu pa 16 February, 2022. […]
The post Aphungu apempha kugulilidwa ma khotholo appeared first on Malawi 24.