Aphungu a DPP atulutsidwa mnyumba ya Malamulo

Aphungu oposa 20 a chipani cha DPP awatulutsa mu nyumba ya malamulo chifukwa anaima kuti alankhule pamene a sipikala anati manja awo ndi omangidwa pa za mtsogoleri wa otsutsa mnyumba ya malamulo ndipo akuona kuti a Kondwani Nankhumwa ndiwo adakali mtsogoleri otsutsa mnyumbayi. Izi zinachitika pamene sipikala wa nyumbayi a Catherine Gotani Hara anawelenga zokambilana […]

The post Aphungu a DPP atulutsidwa mnyumba ya Malamulo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください