Anthu ena apha mayi oyembekezera ndi mamuna wake ku Dedza

Anthu ena dzulo ku Magomero m’boma la Dedza apha mayi oyembekezera ndi mamuna wake ataotcha nyumba yomwe awiriwa amagonamo. Phungu wa delari a Auzious Chidovu watsimikizira wailesi ya Zodiak za nkhaniyi. A Chidovu ati munthu wina adabwereka ndalama kwa banjalo ndipo ndalamayo imamukanika kubweza. Pofuna ndalama zake, bambo amene wamwalirayu anakalanda matumba atatu a chimanga […]

The post Anthu ena apha mayi oyembekezera ndi mamuna wake ku Dedza appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください