Anthu ayamba kulozerana nyumba ya malemu Goodall Gondwe

Nanga inu adzalozerana chiyani mukadzatsamaya? Ndalama osamangodya ngati kuti ndi tomato yemwe mukuopa kuti awola mukakhalitsa naye: anthu uku atutumuka ndi chinyumba cha malemu Goodall Gondwe, ndipo kuli kulozerana kwinaku akuomba m’manja kuti Phuu! Kuli kusavetsetsa ndi zomwe apenya. Anthu ochuluka tchimo lomwe ali nalo ndilosakumbuka kumanga nyumba zokhalamo; osangoti nyumba wamba koma nyumba zomwe […]

The post Anthu ayamba kulozerana nyumba ya malemu Goodall Gondwe appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください