Anthu atatu amangidwa kamba kokupha munthu yemwe anagwidwa akuba nkhuku

Apolisi ku Kasungu atsekera mchitokosi anthu atatu omwe akuwaganizira kuti anapha bambo wa zaka 38 yemwe adamugwira akuba nkhuku. Anthuwa, ndi a Simon Genesis a zaka 40, Kachule Gwilire, a zaka 53 Komanso a Chrisy Genesis a zaka 53, onsewa a m’mudzi mwa a Genesis mfumu yaikulu Kasichi m’bomali. Malingana ndi a Joseph Kachikho omwe […]

The post Anthu atatu amangidwa kamba kokupha munthu yemwe anagwidwa akuba nkhuku appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください