Anthu atatu agwidwa atapezeka ndi Chamba kwa Jenda ku Mzimba

A Polisi akwa Jenda m’boma la Mzimba amanga anthu atatu atawapeza ndi Chamba mdera la Luviri chomwe amafuna apite nacho ku Lilongwe. Mneneri wa a polisi ya Jenda, Sub Inspector Macfarlen Mseteka, wawuza Malawi24 kuti anthuwa adagwidwa akufufuza mayendwe wopita ku Lilongwe mpomwe anthu adatsina khutu a Polisi mderalo. Womwe apalamula mlanduwu ndi mayi Pilirani […]

The post Anthu atatu agwidwa atapezeka ndi Chamba kwa Jenda ku Mzimba appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください