Anthu atatu afa galimoto itagudubuzika

Anthu atatu amwalira pamene anthu ena asanu ndi m’modzi avulala pa ngozi yomwe yachitika dzulo madzulo m’boma la Nkhotakota Yemwe ndi mneneri wa apolisi m’bomali a Sub-Inspector Andrew Kamanga ati galimoto ya mtundu wa Sienta yomwe inanyamula anthuwa inagudubuzika itanyamula anthuwa munsewu wa M5. A Aaron Cement omwe amayendetsa galimotoli komanso wolandira ndalama m’galimotoli ndi […]

The post Anthu atatu afa galimoto itagudubuzika appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください