Anthu achialubino adandaula kuti akumaphedwa kwambiri nthawi yachisankho ikayandikira

ABungwe la achialubino la Association of People Living with Albinism in Malawi (Apam) lati likuda nkhawa ndi chisankho chikubwerachi chifukwa ndi nthawi yomwe amachitiridwa nkhanza kapena kuphedwa kumene. Mkulu wa bungweli a Young Muhamba ndiwo adandaula izi poyankhapo pa nkhani ya manda a munthu wachialubino omwe anafukulidwa ku Mulanje. Apolisi m’boma la Mulanje akufunafuna anthu […]

The post Anthu achialubino adandaula kuti akumaphedwa kwambiri nthawi yachisankho ikayandikira appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください