Anthu 12 avulala pa ngozi ku Blantyre

Anthu khumi ndi awiri, avulala pangozi yomwe inachitika ku Kanjedza-Blantyre pamene minibus yomwe adakwera inalowa mbali yolakwika ndikugunda galimoto ya mtundu wa Corolla isanagunde minibus inanso. Malinga ndi Mneneri wa Polisi ya Limbe, a Aubrey Singanyama, ngoziyi inachitika pafupi ndi malo omwetsela mafuta a Puma ku Blantyre ndipo minibus yomwe inachita ngoziyi imachoka mseu wa […]

The post Anthu 12 avulala pa ngozi ku Blantyre appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください