Anjatidwa kamba kozembetsa matumba 124 a chimanga ku ADMARC

Apolisi m’boma la Nkhotakota amanga mkulu wa za malonda ku Chidewe  ADMARC, Patrick Duston wa zaka 35,  pomuganizira kuti ndi amene anazembetsa matumba 124  achimanga a ndalama zomwana 7.3 miliyoni. Mneneri wa apolisi ya Nkhunga, Andrew Kamanga, wati apolisi analandira lipoti kuchokera ku likulu la ADMARC chigawo chapakati pa 10 February, 2024. “Lipoti likutsindika kuti […]

The post Anjatidwa kamba kozembetsa matumba 124 a chimanga ku ADMARC appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください