Anjatidwa kamba kosayendetsa bwino ndalama

Apolisi m’dziko lino anjata a Shirieesh Betgiri yemwe ndi mkulu wapampando wakale wa kampani ya Salima Sugar kamba kokhudzidwa pa mlandu wakatangale wa ndalama zoposa K50 billion A Peter Kalaya omwe ndi mneneri wa apolisi m’dziko muno atsimikiza zankhaniyi ndipo iwo ati izi zadza pamene boma idachita kafukufuku ndipo malipoti adaonetsa kuti anthu ena adabera […]

The post Anjatidwa kamba kosayendetsa bwino ndalama appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください