Ana sukulu pa Soche Technical achita ziwonesero kamba ati akungodya nyemba basi

Kwavuta ku Soche Technical College ku Blantyre komwe ana a sukulu akutseka misewu kamba kokwiya kuti miyezi ikudusa koma akungolandira zakudya zomwe ndiwo zake ndi nyemba basi. Wachiwiri wa Student Union Council pa sukulupo a Tiyanjane Chisowire wati ndiwodandaula chifuwa ma sabata akwana anayi tsopano chitsegulire sukuluyi koma ndiwo zimangokhala nyemba basi. Mtsogoleri wa sukuluyi […]

The post Ana sukulu pa Soche Technical achita ziwonesero kamba ati akungodya nyemba basi appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください