Ana awiri abanja limodzi afa atadya kalongonda

Ku Kasungu, mnyamata wa zaka zisanu ndi zitatu (8) ndi mchimwene wake wa zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi (16) afa pamene bambo awo ndi mwana wina agonekedwa mchipatala atadya kalongonda kamba ka vuto lakusowa chakudya. Watsimikiza za nkhaniyi ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Kasungu a Joseph Kachikho omwe ati nkhaniyi yachitika m’mudzi mwa […]

The post Ana awiri abanja limodzi afa atadya kalongonda appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください