Amalawi ayamba kukolola zipatso za ulendo wa Chakwera ku Belgium

Amalawi ayamba kukolola zipatso za ulendo wa mtsogoleri wa dziko lino, Dr. Lazarus McCarthy Chakwera, ku dziko la Belgium mchaka cha 2022 pamene makampani a ku dziko la Belgium tsopano ayamba kugwira ntchito zawo mdziko muno. Imodzi mwa makampani omwe Chakwera adakakumana nawo ku Belgium ndi Phillip Morris yomwe Lachinayi yatsimikizira Amalawi za kudzipereka kwake […]

The post Amalawi ayamba kukolola zipatso za ulendo wa Chakwera ku Belgium appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください