Amalawi ambiri ndi mbuli – watero muwulutsi wa pa Mibawa Chawezi Banda

Unyinji unakhamukira ku Njamba lamulungu lija ati si chifukwa chokonda a Mutharika, kapena DPP, kapena kukhumudwa ndi kayendetsedwe ka dziko kamba ka utsogoleri wa Tonse. Ati vuto la onse aja ndi umbuli basi, monga amakhalira a Malawi ochuluka. A Chawezi Banda omwe ndi muwulutsi pa wailesi ya kanema ya Mibawa ndiwo anena izi. Iwo amayankhula […]

The post Amalawi ambiri ndi mbuli – watero muwulutsi wa pa Mibawa Chawezi Banda appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください