Apolisi ku Limbe mumzinda wa Blantyre akusunga mchitokosi bambo wina wa zaka 34 pamene iye ndi azake ena anayi anachitira chiwembu munthu wina woyendetsa njinga yamoto yakabaza ya mtundu wa Lifan LF 150-7 yomwe nambala yake ndi BT 12854 ndicholinga chofuna kumubera. Nkhani yonse ikuti bamboyu yemwe dzina lake ndi Bright Maisa anagwilizana ndi mwini […]
The post Ali mchitokosi kamba kochitira chiwembu wakabaza wa njinga yamoto appeared first on Malawi 24.