Akanganya awili omwe akhala akuchita za umbanda ku Mulanje awanjata

Apolisi ku Mulanje anjata njonda ziwiri zomwe zakhala zikuzinganiziridwa kuti zakhala zikuchita za umbanda mbomali. Mneneri wa apolisi ku Mulanje a Innocent Moses watsimikiza za nkhaniyi ndipo iye wati njonda ziwiri mayina awo ndi a Richard Semu azaka 36 zakubadwa komanso a Joseph Elton azaka 32. Nkhani yonse ikuti apolisi m’bomali anatsinidwa khutu ndi anthu […]

The post Akanganya awili omwe akhala akuchita za umbanda ku Mulanje awanjata appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください