‘Afana otani?’ a Chilima, a Chimwendo, a Matemba ndi ena awatchula pa mndandanda wa okudya za Sattar

Kuganiza bwino ankanena wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino ndikutheka si pa ndale pokha, mwinanso kuchenjela manja kumene. Malipoti ochokela mu dziko la United Kingdom asonyeza kuti a Saulos Chilima ali pa mndandanda wa anthu amene akukayikilidwa kuti akhala akulandila ziphuphu kwa mkulu okayikilidwa za katangale a Zuneth Sattar. Malinga ndi malipoti amene anayalidwa mu […]

The post ‘Afana otani?’ a Chilima, a Chimwendo, a Matemba ndi ena awatchula pa mndandanda wa okudya za Sattar appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください

コメントを残す

メールアドレスが公開されることはありません。 が付いている欄は必須項目です