Adindo adandaula ndikusowa kwa zipangizo zochotsela zinyalala pa msika wa Namadzi

Adindo ena pa msika wa Namadzi ku Chiradzulu adandaula ndikusowa kwa zipangizo zochotsela zinyalala monga mawilibala ndi mafosholo pamsikawu. A George Mkwate m’modzi, wa mamembala a komiti pamsikawu wati mawilibala, mafosholo komanso zotchinga kukamwa ndi zina mwa zinthu zomwe alibiletu pamsikawu. “Kusowa kwa zinthu zimenezi kumaika moyo wathu pa chiopsezo cha matenda osiyanasiyana,” adatero a […]

The post Adindo adandaula ndikusowa kwa zipangizo zochotsela zinyalala pa msika wa Namadzi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください