Achinyamata ena 200 wapsa wa ku Israel mawa

Boma latsimikiza kuti gulu la chiwiri la achinyamata okwana 200 linyamuka m’dziko muno lachitatu kupita kukagobola ntchito zakumunda m’dziko la Israel. Watsimikiza za nkhaniyi ndi ofalitsa nkhani ku unduna wazantchito a Nellie Kapatuka omwe awuza nyumba zina zofalitsa nkhani m’dziko muno kuti ndege yomwe ikuyembekezeka kunyamula anthuwa, ifika m’dziko muno lero lachiwiri masana ano Malingana […]

The post Achinyamata ena 200 wapsa wa ku Israel mawa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください