Abambo atatu anjatidwa kamba kopha mulamu wawo

Abambo atatu ali m’manja mwa apolisi mu mzinda wa Lilongwe powaganizira kuti adapha ndi kukwilira mwa chinsinsi mulamu wawo a Luciano Masiye a zaka 26. Malingana ndi mneneli wa Polisi ya Lilongwe a Hastings Chigalu, izi zidachitika m’mudzi mwa Lumwila m’bomali, ndipo a Chigalu atsimikiza kuti atatuwa ndi a Polofesa Posiyano a zaka 24, a […]

The post Abambo atatu anjatidwa kamba kopha mulamu wawo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください