A Uladi Mussa alowa MCP: Ati “Fotseki DPP”

Patangodutsa ma sabata ochepa chipani Cha Democratic Progressive Party DPP chitachotsa kamanso kuimika ena mwa ma Membala ake omwe m’modzi mwa iwo ndi a Uladi Mussa, iwo tsopano ati alowa chipani cha Malawi Congress ponena kuti iwo akana chibwana Cha ku DPP. A Mussa awonetsedwa ku guru ndi wachiwiri kwa mulembi wa chipani cha MCP […]

The post A Uladi Mussa alowa MCP: Ati “Fotseki DPP” appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください