A Nankhumwa sangakatiwinitse ku chisankho za 2025, atero a Namalomba

M’modzi wa akuluakulu a chipani cha DPP a Shadric Namalomba ati mtsogoleri wa zipani zotsutsa boma Kondwani Nankhumwa sangakawanitse chipanichi ku chisankho cha 2025 ndi chifukwa chake iwo akufuna mtsogoleri wakale wa dziko lino a Peter Mutharika kuti akayimire DPP ndi cholinga choti chipanichi chilowenso m’boma. A Nankhumwa anawonetsa chidwi chozapikisana ndi a Mutharika pa […]

The post A Nankhumwa sangakatiwinitse ku chisankho za 2025, atero a Namalomba appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください