A Mutharika achezera Asilamu pa Mzikiti wa Mangochi main, agawa zakudya zambiri

Mtsogoleri wakale wa dziko lino yemwenso ndi Mtsogoleri wa Chipani cha Democratic Progressive Party-DPP, His Excellency Professor Arthur Peter Mutharika, lero chakusanaku anakachezera asilamu pa Mzikiti wa Mangochi Main Mosque ntown ya Mangochi. Mwachizowezi, a Mutharika anachezera komanso kuwalimbikisa abale ndi alongo achisilamu amene padakali pano ali mu nyenyo Ramadan. Iwo ananena kuti nyenyo ya […]

The post A Mutharika achezera Asilamu pa Mzikiti wa Mangochi main, agawa zakudya zambiri appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください