A Ken Msonda apepesa kwa a Mutharika

A Ken Msonda omwe ndi membala wa komitiyi yaikulu ya chipani cha DPP apepesa kwa mtsogoleri wa chipanichi a Peter Mutharika pa zomwe iwo akhala akuchita ndipo pano ati akufuna a Mutharika atengenso mpando wa mtsogoleri wa chipani cha DPP. Izi zadza pomwe lero a Mutharika anayankhula mozaza ndikuwadzudzula a Msonda kuti akhoza kubwerela ku […]

The post A Ken Msonda apepesa kwa a Mutharika appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください