A ‘City’ ayenda wa uyo-uyo ku Limbe

Kunali phazi thandize ku Limbe mu mzinda wa Blantyre pomwe ochita malonda m’mphepete mwa misewu anavumbulutsa miyala ndipo nawo ogendawo anafukizidwa komaso kuwubwira utsi okhetsa misozi. Izi zachitika lachiwiri pa 21 November, 2023 pomwe monga mwa nthawi zonse akuluakulu ochokera ku khonsolo ya Blantyre anapita mu msika wa Limbe kuti akathane ndi anthu onse omwe […]

The post A ‘City’ ayenda wa uyo-uyo ku Limbe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください