Chakwera watsimikizira aMalawi kuti ngozi ya ndege ifufuzidwa mosabisa komanso mwapadera

Mtsogoleri wa dziko lino Dr. Lazarus McCarthy Chakwera watsimikizira aMalawi ndi mayiko onse akunja kuti boma lake liwonetsetsa kuti ngozi ya ndege ifufuzidwa mosabisa komanso mwapadera pofuna kuti chilungamo chidziwike. Chakwera wanena izi pa Bingu National Stadium mu mzinda wa Lilongwe pa mwambo wokhudza maliro a yemwe anali wachiwiri wake, Dr. Saulos Klaus Chilima. Chilima […]

The post Chakwera watsimikizira aMalawi kuti ngozi ya ndege ifufuzidwa mosabisa komanso mwapadera appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください