Bungwe lobwerekesa ndalama la NEEF lapempha Akhristu mdziko muno kuti azibwedza ngongole

Bungwe la boma lobweleketsa ngongole la (NEEF) lapempha a khristu kuti adzibweza ngongole zomwe amatenga ku bungweli komanso mabungwe ena opereka ngongole. Mmodzi mwa akuluakulu owona nkhanizi a Humphrey Thondolo, ndiye wanena izi Lamulungu madzulo pa mpingo wa Area 25 Assemblies of God pa maphunziro okhudza mene ndondomeko ya ngongole imayendera.   Malinga ndi a […]

The post Bungwe lobwerekesa ndalama la NEEF lapempha Akhristu mdziko muno kuti azibwedza ngongole appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください