Kwa Nkope ku Mangochi kuli chiopsezo cha matenda otsegula mimba

Anthu omwe akhudzidwa ndi kusefukila kwa madzi ku Nkope m’boma la Mangochi ati miyoyo yawo ili pa chiopsezo chodwala matenda otsekula mmimba ngakhale kufa ndi njala kumene. Anthu-wa omwe akukhala ku misasa ati nyumba zawo, zimbuzi, chakudya mwa zina zinaonongeka ndipo akusowekera thandizo la msangasanga. Iwo ati akumwa madzi osatetezeka komanso anthu akumangozithandiza paliponse kaamba […]

The post Kwa Nkope ku Mangochi kuli chiopsezo cha matenda otsegula mimba appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください