Khonsolo ya mzinda wa Lilongwe m’bandakucha wa lero yagwetsa nyumba zomwe anthu ena anamanga ku Malangalanga mu mzinda wa Lilongwe. Malingana ndi mneneri wa khonsoloyi a Tamara Chafunya, nyumba zina zomwe eni ake anatenga chiletso ku khothi kuti asawagwetsere, azisiya kaye pakadali pano. Iwo ati ntchitoyi akhala akuyigwira m’malo ochitira malonda komanso okhala anthu, ngakhale […]
The post Khonsolo ya Lilongwe yayamba kugwesa ma shop omangidwa malo osalolezedwa m’muzindawu appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.