Aford yasindika kuti izayima payokha ndipo yanenetsa kuti izatenga upulezidenti wa dziko lino

Chipani cha Alliance for Democracy (Aford) chati chili ndi chikhulupiliro kuti chidzapambana chikadzaima pa chokha pa chisankho cha mtsogoleri wa dziko cha chaka cha mawa. Wofalitsa nkhani za chipanichi a Amatullah Annie Maluwa auza Nyasatimes kuti kwa zaka zitatu tsopano chipanichi chakula mphamvu zimene zikupereka chirimbikitso kuti chidzaime pa chokha. A Maluwa ati kutuluka kwa […]

The post Aford yasindika kuti izayima payokha ndipo yanenetsa kuti izatenga upulezidenti wa dziko lino appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください