Pakali pano tafikira anthu oposa 700 000 ndi chimanga chaulere, atero Bushiri

Prophet Shepherd Bushiri wati pakali pano ntchito yawo yogawa chimanga chaulere kwa a Malawi omwe akhuzidwa ndi ngozi zadzidzidzi yikupitilirabe ndipo panopa afikira anthu oposa 700 000. Mneneri wa a Bushiri a Aubrey Kusakala anena izi ku Mangochi komwe athandiza mabanja oposa 200 mdera la Senior Chief Nankumba ku Monkey-Bay m’boma la Mangochi. A Bushiri […]

The post Pakali pano tafikira anthu oposa 700 000 ndi chimanga chaulere, atero Bushiri appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください