Anthu alimbikitsidwa kugwiritsa ntchito njira zingapo zopewera kutenga HIV

Pomwe zotsatira za kafukufuku zasonyeza kuti anthu opitilira 15,000 ndi omwe anatenga kachirombo ka HIV chaka chatha chokha, akatswiri ati kugwiritsa ntchito njira zingapo zopewera kutenga kachiromboka, kungathandize kuchepetsa chiwerengerochi. Izi ndi malingana ndi a Ulanda Mtamba omwe ndi wa chiwiri kwa mtsogoleri wa bungwe la Civil Society Advocacy Forum omwenso ndi m’modzi mwa akatswiri […]

The post Anthu alimbikitsidwa kugwiritsa ntchito njira zingapo zopewera kutenga HIV appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください