Nduna yakale ya za masewero mu ulamuliro wachipani cha UDF yamwalira

Nduna yakale ya za masewero mu ulamuliro wachipani cha United Democratic Front (UDF) a Moses Dossi yamwalira. Mwana wamalemuwa Susan wati a Dossi amwalira kuchipatala cha Blantyre Adventist kucha kwa Lachinayi ali ndi zaka 70 ndipo wati adzawakumbikira bambo wake chifukwa adali munthu okonda mtendere komanso okonda aliyense. A Dossi, omwenso adakhalapo phungu wakunyumba yamalamulo […]

The post Nduna yakale ya za masewero mu ulamuliro wachipani cha UDF yamwalira appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください