Awiri anjata pofuna kulowetsa chamba ku ndende

Mnyamata wina yemwe amayankha mlandu kale, wamangidwaso kachiwiri pamodzi ndi mzake wina yemwe amafuna kukamupatsira chamba chomwe anachibisa munkhwayira tsiku lakumva mlandu. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa Polisi ya Zomba, a Patricia Supuliano, oganizilidwa awiriwa ndi Estery Evance wa zaka 19 komaso Bonface Phiri wa zaka 22.  A Supuliano ati izi zachitika Lachiwiri pa 16 […]

The post Awiri anjata pofuna kulowetsa chamba ku ndende appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください