Alimi muyenera kulondoloza fodya wanu kuti ena asalemelere ndi umbava otibera -atero a Chakwera

President wa dziko lino, a Lazarus Chakwera, ati alimi akuyenera kulondoloza fodya wawo moyenera cholinga choti ena asalemere powabera alimiwa potengera kuti ulimi wa fodya umafunika chidwi komanso kulondoloza chilichonse mu nthawi yoyenera. A Chakwera anena izi pa msonkhano omwe anapangitsa pa sukulu ya pulayimale ya Vivya kwa mfumu yaikulu Njombwa ku Kasungu pomwe amatsegurira […]

The post Alimi muyenera kulondoloza fodya wanu kuti ena asalemelere ndi umbava otibera -atero a Chakwera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください