Bambo wina wa zaka 32 ku Blantyre, ali muululu owopsya pa chipatala cha Queen Elizabeth munzinda wa Blantyre pomwe wavulazidwa ndi nyesi za magetsi pomwe akuganizilidwa kuti amafuna kuba mawaya a magetsi. Malingana ndiwofalitsa nkhani pa polisi ya Limbe, Sergeant Aubrey Singanyama, bambo oganizilidwa kubayu wazindikilidwa ngati a Dickson Khoviwa omwe akuti akumana ndi zakudazi […]
The post Mbava yavulazidwa ndi nyesi ikuba mawaya a magetsi appeared first on Malawi 24.
Moni Malawi 