Ma Mega Farm ayambikadi: Kawale akhutisidwa ndi kupita patsogolo kwa Mlambe Mega Farm ku Mangochi

Unduna wa zaulimi wati ukupitiliza kukwanilitsa masomphenya a pulezidenti Lazarus Chakwera oonetsetsa kuti njala itheretu mdziko muno polima zakudya kudzela mu ulimi othilira. Izi anena ndi nduna ya za ulimi a Sam Kawale lero atayendera mmene ntchito yokonzaso Mlambe Mega Farm ikuyendela ku Nkopola, Mangochi. “Mega Farm imeneyi ndi ya ma hekita 800 ndipo ma […]

The post Ma Mega Farm ayambikadi: Kawale akhutisidwa ndi kupita patsogolo kwa Mlambe Mega Farm ku Mangochi appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください