Kamlepo ayambitsa phokoso ku Parliament atadzudzula boma kuti sililabadira anthu aku mpoto

Ku nyumba ya malamulo kunabuka chipwirikiti masanawa, zomwe zidapangitsa kuti Kamlepo Kalua, phungu wa dera la ku mmawa m’boma la Rumphi komanso Christopher Manja phungu wa dera la ku m’mwera kwa boma la Salima atulusidwe mnyumbayi. Kalua anadzudzula boma lotsogozedwa ndi Tonse kuti silisamala chigawo chakumpoto pa ntchito zachitukuko ponena kuti boma lapereka ndalama zokwana […]

The post Kamlepo ayambitsa phokoso ku Parliament atadzudzula boma kuti sililabadira anthu aku mpoto appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください