Potsatira kalata yomwe Zani Challe anatulutsa yodandaula komaso kuopseza kuti apanga chinthu china chomwe sananene pa Tuno kamba komunena kuti iye amagulitsa thupi komaso amachita malonda a mankhwala ozunguza ubongo, oyimbayu wapepesa tsopano. Nkhaniyi inayamba Lachiwiri usiku pomwe oyimba Tuno yemwe anabadwa Tunosiwe Mwakalinga amacheza mu pologalamu ya ‘Truth or Drink’ yomwe limapangitsa ndi gulu […]
The post Nkhondo siimanga mudzi: Tuno wapepesa Zani Challe appeared first on Malawi 24.