Sukulu za pulayimale zomwe ophunzira amuna akuvala ma buluku ngati yunifolomu azichenjeza

Sukulu za pulayimale za boma zomwe ophunzira ake amuna anayamba kale kuvala ma yunifolomu a ma buluku, zachenjezedwa ndi unduna wa maphunziro kuti zisiye ponena kuti pakadali pano lamuloli silinakhazikitsidwe. Chaka chatha, phungu wa nyumba ya malamulo ochokera m’dera la Zomba Thondwe, a Roseby Gadama anapeleka maganizo m’nyumba ya malamulo kuti boma la Malawi liyambe […]

The post Sukulu za pulayimale zomwe ophunzira amuna akuvala ma buluku ngati yunifolomu azichenjeza appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください