Chithyola akhazikisa ntchito yopereka ndalama kwa anthu ovutika okhala m’matauni: Anthu ayamba kulandira

Nduna yoona zachuma Simplex Chithyola- Banda watsindika kuti anthu amene amakhala m’matauni nawonso amakumana ndi umphawi wa dzaoneni. A Chithyola-Banda anena izi m’boma la Zomba pa mwambo okhazikitsa ndondomeko ya mtukula pakhomo wa m’mizinda ya Zomba, Blantyre, Lilongwe komanso Mzuzu. Malingana ndi ndunayi,ndi mtukula pakhomowu, umene ukuthandizidwa ndi a World Bank, mabanja okwana 105 000 […]

The post Chithyola akhazikisa ntchito yopereka ndalama kwa anthu ovutika okhala m’matauni: Anthu ayamba kulandira appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください