Chakwera wauza unduna wa zamaphunziro kuti uwunikenso ndalama za ophunzira ku koleji amalandira

Mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera wauza Unduna wa Zamaphunziro kuti uwunikenso ndalama zomwe ophunzira mu sukulu za ukachenjede amalandira pamwezi kuti zikwezedwe. A Chakwera ati ophunzira mu sukulu za ukachenjede asamasowe zofunikira pa moyo wawo monga sopo, kuti aziika chidwi chawo chonse pa maphunziro. A Chakwera anena izi pa sukulu ya ukachenjede ya Malawi […]

The post Chakwera wauza unduna wa zamaphunziro kuti uwunikenso ndalama za ophunzira ku koleji amalandira appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください