Nzika zokhudzidwa zichita m’bindikilo ku maofesi onse a Immigration

Anthu ena omwe akudzitchula kuti nzika zokhudzidwa ati achita m’bindikilo kuma ofesi onse a nthambi yowona zolowa ndi zotuluka ya DICS pofuna kukakamiza mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera kuti achotse ntchito mkulu wa nthambiyi komaso nduna yokhudzidwa. Izi ndi malingana ndi chikalata chomwe nzika za nchigawo chakum’mwera zalembera khonsolo ya mnzinda wa Blantyre […]

The post Nzika zokhudzidwa zichita m’bindikilo ku maofesi onse a Immigration appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください